Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 158
  • “Sadzachedwa”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Sadzachedwa”
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Mukhoza Kuyembekezera Moleza Mtima?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2017
  • Tsanzirani Kuleza Mtima kwa Yehova ndi Yesu
    Nsanja ya Olonda—2012
  • Pitirizani Kukhala Oleza Mtima
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2023
  • Kodi Mungasonyeze Kuleza Mtima?
    Nsanja ya Olonda—1994
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 158

NYIMBO 158

“Sadzachedwa”

Losindikizidwa

(Habakuku 2:3)

  1. 1. Dziko lopanda

    nkhawa zonsezi

    Ndi lomwe tonse

    tikulakalaka.

    Padziko lonse

    zinthu zaipa

    Tikudziwatu

    muthetsa zonsezi.

    (KOLASI)

    Molezadi mtima

    tikudikirira

    Dzikotu latsopano.

    Mapeto afika

    posachedwa pompa.

    Mawu anu akuti,

    ‘sadzachedwadi.’

  2. 2. Mulungu wathu

    mudzaitana

    Omwe anafa, ndipo

    adzadzuka.

    Zidzakhalatu

    zosangalatsa!

    Tithandizeni

    kulezabe mtima.

    (KOLASI)

    Molezadi mtima

    tikudikirira

    Dzikotu latsopano.

    Mapeto afika

    posachedwa pompa.

    Mawu anu akuti,

    ‘sadzachedwadi.’

  3. 3. Mumafufuza

    mitima yathu

    N’kutitonthoza ndi

    chiyembekezo.

    Tichite khama

    polalikira.

    Tikhale maso

    nthawi yafupika.

    (KOLASI)

    Molezadi mtima

    tikudikirira

    Dzikotu latsopano.

    Mapeto afika

    posachedwa pompa.

    Mawu anu akuti,

    ‘sadzachedwadi.’

    Tiyembekezerebe.

(Onaninso Akol. 1:11.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena