Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • CO-pgm24 tsamba 4-5
  • Loweruka

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Loweruka
  • Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2024
  • Nkhani Yofanana
  • Lachisanu
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2024
  • Lachisanu
    Pulogalamu ya Msonkhano wa 2025
  • Loweruka
    Pulogalamu ya Msonkhano wa 2025
  • Loweruka
    Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2022
Onani Zambiri
Pulogalamu ya Msonkhano Wachigawo wa 2024
CO-pgm24 tsamba 4-5
Zithunzi: Zimene zili mupulogalamu ya Loweruka. 1. Yosefe ndi Mariya ali ndi Yesu. 2. Mfumu Herode. 3. Mabanja awiri a Mboni ali muutumiki.

Loweruka

“Tsiku ndi tsiku muzilengeza uthenga wabwino wa chipulumutso chake”​—Salimo 96:2

M’mawa

  • 8:20 Kuonera Vidiyo ya Nyimbo

  • 8:30 Nyimbo Na. 53 Komanso Pemphero

  • 8:40 ‘Ndikuyenera . . . Kulengeza Uthenga Wabwino wa Ufumu’ (Luka 4:43)

  • 8:50 VIDIYO:

    Uthenga Wabwino wa Yesu: Gawo 1

    Kuwala Kwenikweni kwa Dziko​—Mbali Yachiwiri (Mateyu 2:1-23; Luka 2:1-38, 41-52; Yohane 1:9)

  • 9:25 Nyimbo Na. 69 Komanso Zilengezo

  • 9:35 NKHANI YOSIYIRANA: Kukwaniritsidwa kwa Maulosi Onena za Mesiya

    • • Kunabwera Mthenga Iye Asanabwere (Malaki 3:1; 4:5; Mateyu 11:10-14)

    • • Anabadwa kwa Namwali (Yesaya 7:14; Mateyu 1:18, 22, 23)

    • • Anabadwira ku Betelehemu (Mika 5:2; Luka 2:4-7)

    • • Anatetezedwa Ali Mwana (Hoseya 11:1; Mateyu 2:13-15)

    • • Anatchedwa Mnazareti (Yesaya 11:1, 2; Mateyu 2:23)

    • • Anaonekera pa Nthawi Yoikidwiratu (Danieli 9:25; Luka 3:1, 2, 21, 22)

  • 10:40 NKHANI YA UBATIZO: Pitirizani ‘Kugonjera Uthenga Wabwino’ (2 Akorinto 9:13; 1 Timoteyo 4:12-16; Aheberi 13:17)

  • 11:10 Nyimbo Na. 24 Komanso Kupuma

Masana

  • 12:35 Kuonera Vidiyo ya Nyimbo

  • 12:45 Nyimbo Na. 83

  • 12:50 NKHANI YOSIYIRANA: Muzigwiritsa Ntchito Uthenga Wabwino Kuti Mugonjetse Uthenga Oipa

    • • Miseche (Yesaya 52:7)

    • • Kuvutika ndi Chikumbumtima (1 Yohane 1:7, 9)

    • • Zochitika za Masiku Ano (Mateyu 24:14)

    • • Zinthu Zofooketsa (Mateyu 11:28-30)

  • 1:35 NKHANI YOSIYIRANA: ‘Muzikhala Ofunitsitsa Kulalikira Uthenga Wabwino’

    • • Sinali Ntchito ya Atumwi Okha (Aroma 1:15; 1 Atesalonika 1:8)

    • • Ndi Mbali ya Kulambira (Aroma 1:9)

    • • Muzikonzekera Komanso Kugwiritsa Ntchito Zinthu Zoyenera (Aefeso 6:15)

  • 2:15 VIDIYO: Mmene ‘Uthenga Wabwino Ukubalira Zipatso Komanso Kufalikira Padziko Lonse’ (Akolose 1:6)

  • 2:40 Nyimbo Na. 35 Komanso Zilengezo

  • 2:50 NKHANI YOSIYIRANA: Pitirizani Kulalikira Uthenga Wabwino

    • • Kulikonse Komwe Muli (2 Timoteyo 4:5)

    • • Kulikonse Komwe Mulungu Akufuna (Machitidwe 16:6-10)

  • 3:15 Kodi Mudzachita Chiyani “Chifukwa cha Uthenga Wabwino”? (1 Akorinto 9:23; Yesaya 6:8)

  • 3:50 Nyimbo Na. 21 Komanso Pemphero Lomaliza

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena