Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 11/14 tsamba 3
  • “Ndikapita Sindiwapeza”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Ndikapita Sindiwapeza”
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Nkhani Yofanana
  • Tizichita Maulendo Obwereza kwa Anthu Amene Anasonyeza Chidwi
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2011
  • Kuwonjezera Luso Lathu mu Utumiki​— Kulalikira Pogwiritsa Ntchito Foni
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2020
  • Bwererani kwa Onse Amene Asonyeza Chidwi Ngakhale Chochepa
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2006
  • Kuwonjezera Luso Lathu mu Utumiki—Muzisiya Funso Loti Mudzakambirane pa Ulendo Wotsatira
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
Onani Zambiri
Utumiki Wathu wa Ufumu—2014
km 11/14 tsamba 3

“Ndikapita Sindiwapeza”

Kodi munayamba mwanenapo mawu amenewa ponena za munthu wina yemwe anaonetsa kuti ali ndi chidwi? Kusapezanso munthu wotereyu kungapangitse kuti mulephere kuthirira mbewu za choonadi zomwe munadzala. (1 Akor. 3:6) Ofalitsa ena akapita kangapo kunyumba ya munthu wachidwi amene anacheza naye koma osam’peza, amalemba kakalata n’kumusiyira panyumba yake kapena amakalemba kalata n’kumutumizira. Ofalitsa ena akaona kuti mwina sadzam’pezanso munthuyo pakhomo, amamupempha nambala ya foni yake n’kumufunsa kuti, “Ndingadzakulembereni meseji?” Tingawerengere ulendo wobwereza ngati talalikira munthu pogwiritsa ntchito kalata, imelo, meseji kapena kumuimbira foni. Njira zimenezi zingathandize kuti tipitirizebe kukambirana ndi munthu wachidwi ngakhale kuti sakupezeka pakhomo.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena