Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 2/15 tsamba 4
  • Muzidzipereka Polimbikitsa Ena Kuchita Zabwino

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Muzidzipereka Polimbikitsa Ena Kuchita Zabwino
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Nkhani Yofanana
  • Tiziganizirana Ndiponso Kulimbikitsana
    Nsanja ya Olonda—2013
  • Fulumizanani ku Chikondano ndi Ntchito Zabwino—MotanI?
    Nsanja ya Olonda—1995
  • Misonkhano Imafulumiza ku Ntchito Zabwino
    Utumiki Wathu wa Ufumu—1997
  • “Khalani Ochuluka mu Ntchito Zabwino”
    Utumiki wathu wa Ufumu—2002
Onani Zambiri
Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
km 2/15 tsamba 4

Muzidzipereka Polimbikitsa Ena Kuchita Zabwino

Lemba la Aheberi 10:24 limatiuza kuti, “tiganizirane kuti tilimbikitsane pa chikondi ndi ntchito zabwino.” Abale ndi alongo athu angalimbikitsidwe akaona chitsanzo chathu chabwino komanso zinthu zosonyeza chikhulupiriro zimene timachita. Choncho, muziuza ena zinthu zolimbikitsa zomwe mwakumana nazo. Athandizeni kuona kuti mukusangalala kwambiri kutumikira Yehova. Koma mukamachita zimenezi, pewani kuwayerekezera ndi ena kapena ndi inuyo. (Agal. 6:4) Cholinga chanu chikhale kuwalimbikitsa pa “chikondi ndi ntchito zabwino,” osati kuwachititsa kuti azidziimba mlandu. (Onani buku la Sukulu ya Utumiki tsamba 158, ndime 4.) Tikamakondana, zingakhale zosavuta kuti tizithandizana komanso kuti tizigwira bwino ntchito yolalikira.​—2 Akor. 1:24.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena