Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 4/15 tsamba 4
  • Muzilengeza za Mphamvu ya Mawu a Mulungu mu Utumiki

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Muzilengeza za Mphamvu ya Mawu a Mulungu mu Utumiki
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Nkhani Yofanana
  • Mawu Akumapeto
    Zimene Baibulo Limaphunzitsa
  • ‘Mawu a Mulungu Ndi Amphamvu’
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2017
  • Thandizani Ophunzira Baibulo Kuyamikira Makhalidwe Osayerekezereka a Yehova
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2006
  • Mmene Mungayambitsire Maphunziro M’buku la Baibulo Limaphunzitsa Chiyani
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2006
Onani Zambiri
Utumiki Wathu wa Ufumu—2015
km 4/15 tsamba 4

Muzilengeza za Mphamvu ya Mawu a Mulungu mu Utumiki

Ngati munthu wavomera kuti timuuze uthenga wabwino, tiyenera kugwiritsa ntchito mpata umenewo kulengeza za mphamvu ya Mawu a Mulungu. Tingachite zimenezi powerenga naye Baibulo. Mfundo imeneyi inafotokozedwa bwino pa msonkhano wadera wa chaka chatha. Woyang’anira dera anakamba nkhani ya mutu wakuti, “Muzilengeza za Mphamvu ya Mawu a Mulungu mu Utumiki.” Kodi mukukumbukira mfundo zomwe zinakambidwa m’nkhaniyi?

  • N’chifukwa chiyani Mawu a Yehova ndi amphamvu kwambiri kuposa mawu athu?—2 Tim. 3:16, 17.

  • Kodi Mawu a Mulungu amathandiza bwanji anthu kusintha mmene amaganizira, zolinga zawo, zimene amakhulupirira ndiponso khalidwe lawo?—Onani Nsanja ya Olonda ya June 15, 2012, tsamba 27 ndime 7.

  • Tikawerenga Baibulo ndi munthu mu utumiki, kodi tingamuthandize bwanji kuti aziona kuti Mawu a Mulungu ndi othandiza kwambiri?—Onani buku la Sukulu ya Utumiki tsamba 148 ndime 3-4 komanso Utumiki Wathu wa Ufumu wa March 2013, tsamba 6 ndime 8.

  • N’chifukwa chiyani n’zofunika kuti tizifotokoza komanso kukambirana ndi munthu malemba amene tawerenga ndipo tingachite bwanji zimenezi?—Mac. 17:2, 3; onaninso buku la Sukulu ya Utumiki tsamba 154 ndime 4 mpaka tsamba 156 ndime 5.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena