Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb17 June tsamba 1
  • Zitsanzo za Ulaliki

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zitsanzo za Ulaliki
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Timitu
  • Nkhani Yofanana
  • GALAMUKANI!
  • KUPHUNZITSA CHOONADI
  • KODI N’CHIYANI CHINGATHANDIZE KUTI BANJA LIKHALE LOSANGALALA?
  • LEMBANI ULALIKI WANUWANU
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Zitsanzo za Ulaliki
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
mwb17 June tsamba 1
Mlongo akuphunzira Baibulo komanso kusinkhasinkha

Mlongo akuphunzira Baibulo komanso kusinkhasinkha

Zitsanzo za Ulaliki

GALAMUKANI!

Galamukani! Na. 3 2017 | Kodi Baibulo ndi Lochokeradi kwa Mulungu?

Funso: Kodi Baibulo ndi mawu ochokeradi kwa Mulungu? Kapena mumaliona ngati buku lomwe munangolembedwa maganizo a anthu?

Lemba: 2 Tim. 3:16

Perekani Magaziniyo: Galamukani! iyi ikufotokoza zinthu zitatu zotsimikizira kuti Baibulo linachokeradi kwa Mulungu.

KUPHUNZITSA CHOONADI

Baibulo lotsegula

Funso: Kodi tiyenera kuiona bwanji mphatso ya moyo?

Lemba: Chiv. 4:11

Zoona Zake: Popeza moyo ndi mphatso yochokera kwa Mulungu, timaulemekeza kwambiri. Timayesetsa kupewa ngozi ndipo sitingachite mwadala zinthu zilizonse zimene zingawononge moyo wa munthu wina chifukwa timadziwa kuti moyo ndi mphatso yamtengo wapatali.

KODI N’CHIYANI CHINGATHANDIZE KUTI BANJA LIKHALE LOSANGALALA?

Kodi N’chiyani Chingathandize Kuti Banja Likhale Losangalala?

Funso: Taonani funso limene lili pa kapepalaka komanso mayankho amene aperekedwa. Kodi inuyo mungayankhe bwanji?

Lemba: Luka 11:28

Perekani Kapepalako: Kapepalaka kakufotokoza zimene banja lanu lingachite kuti lizikhala losangalala komanso chifukwa chake tiyenera kukhulupirira zimene Baibulo limanena.

LEMBANI ULALIKI WANUWANU

Potengera zitsanzozi, konzani njira imene mungagwiritse ntchito.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena