Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb18 May tsamba 7
  • Pewani Msampha Woopa Anthu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Pewani Msampha Woopa Anthu
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Nkhani Yofanana
  • Anawakonzekeretsa Kuti Azilalikira Ngakhale Pamene Akuzunzidwa
    Yesu—Ndi Njira, Choonadi ndi Moyo
  • “Ndakupatsani Chitsanzo”
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Zimene Zingatithandize Kuthetsa Mantha
    Phunzirani kwa Mphunzitsi Waluso
  • Akonda Tiana
    Bukhu Langa la Nkhani za Baibulo
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
mwb18 May tsamba 7

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | MALIKO 13-14

Pewani Msampha Woopa Anthu

N’chifukwa chiyani atumwi anakodwa mumsampha woopa anthu?

14:29, 31

  • Ankadzidalira kwambiri. Mwachitsanzo Petulo ankaona kuti iyeyo adzakhalabe wokhulupirika kwa Yesu kuposa atumwi enawo

    Petulo akukana Yesu

14:32, 37-41

  • Iwo analephera kukhalabe maso komanso anasiya kupemphera

    Atumwi akugona pamene Yesu akupemphera

Yesu ataukitsidwa, n’chiyani chinathandiza atumwi kuti asamaope anthu n’kumalalikirabe ngakhale kuti ankatsutsidwa?

13:9-13

  • Anamvera machenjezo a Yesu ndipo zotsatira zake analimba mtima pamene ankatsutsidwa komanso kuzunzidwa

  • Anadalira Yehova komanso anapemphera.​—Mac. 4:24, 29

    Petulo ndi Yohane ali m’bwalo la Sanihedirini

Kodi ndi zochitika ziti zimene zingachititse kuti kulimba mtima kukhale kovuta?

Mayi wa Mboni ali m’chipatala ndipo akukambirana ndi dokotala; mnyamata wa Mboni ali m’kalasi ndipo sakuchitira nawo saluti mbendera; wa Mboni akulandira khadi yomuitanira kuphwando la kuntchito
    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena