Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb19 February tsamba 2
  • Pitirizani Kuphunzitsa Chikumbumtima Chanu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Pitirizani Kuphunzitsa Chikumbumtima Chanu
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Mungatani Kuti Mukhalebe ndi Chikumbumtima Chabwino?
    Kodi Mungatani Kuti ‘Mulungu Apitirize Kukukondani’?
  • Mungatani Kuti Muzikhala Ndi Chikumbumtima Chabwino?
    Kodi Mungatani Kuti Mulungu Azikukondani?
  • Muziphunzitsa Chikumbumtima Chanu ndi Malamulo Komanso Mfundo za Mulungu
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2018
  • Kodi Muli ndi Mtima Wofewa Ngati Mnofu?
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
mwb19 February tsamba 2

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | AROMA 1-3

Pitirizani Kuphunzitsa Chikumbumtima Chanu

M’bale akuganizira zimene akuwerenga pamene akuphunzira payekha

2:14, 15

Chikumbumtima chathu chingatithandize kusankha bwino zochita ngati . . .

  1. timachiphunzitsa pogwiritsa ntchito mfundo za m’Baibulo

  2. timachimvera chikamatikumbutsa mfundozo

  3. timapempha mzimu woyera kuti utithandize kulimbana ndi matupi athu ochimwawa.​—Aroma 9:1

Kodi ndi mfundo za m’Baibulo ziti zimene ndiyenera kumazigwiritsa ntchito . . .

  • Banja likukana mowa

    pa nkhani ya kumwa kapena kusamwa mowa?

  • Mlongo wachitsikana akusankha chovala

    pa nkhani ya zovala komanso kudzikongoletsa?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena