Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb19 July tsamba 2
  • Vulani Umunthu Wakale N’kuvala Umunthu Watsopano

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Vulani Umunthu Wakale N’kuvala Umunthu Watsopano
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Nkhani Yofanana
  • Mukhoza ‘Kuvula Umunthu Wakale’
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2022
  • “Mawu a Mulungu Ngamoyo Ndipo Amapereka Mphamvu”
    Nsanja ya Olonda​—1990
  • Pitirizani Kuvala “Umunthu Watsopano” Pambuyo Pobatizidwa
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2022
  • Kodi Mumafuna Mutakhala Munthu Wotani?
    Nsanja ya Olonda—2008
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
mwb19 July tsamba 2

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | AKOLOSE 1-4

Vulani Umunthu Wakale N’kuvala Umunthu Watsopano

3:5-14

Mlongo watsegula Baibulo lake ndipo akuganizira mfundo zimene wawerenga m’buku la Yandikirani kwa Yehova

Kodi mutaphunzira choonadi munasintha makhalidwe amene munali nawo poyamba? Musamakayikire kuti Yehova anasangalala chifukwa cha khama limene munasonyeza kuti musinthe. (Ezek. 33:11) Komabe mumafunika kuyesetsa kuti musayambirenso kuchita makhalidwe oipa komanso kuti mupitirize kusonyeza umunthu watsopano. Yankhani mafunso ali m’munsiwa kuti mudziwe mbali zimene mukufunikira kusintha:

  • Kodi ndimasungirabe chakukhosi munthu wina yemwe anandilakwira?

  • Kodi ndimachita zinthu modekha ngakhale zitakhala kuti ndikufulumira komanso ndatopa?

  • Kodi ndikayamba kuganizira zinthu zolakwika ndimasintha n’kuyamba kuganizira zinthu zabwino?

  • Kodi ndimadana ndi anthu ena chifukwa cha mtundu wawo kapena kumene anachokera?

  • Kodi chaposachedwapa ndinapsa mtima kapena kulankhula mawu achipongwe kwa munthu wina?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena