Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb21 March tsamba 12
  • Yehova Amasintha Temberero N’kukhala Dalitso

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yehova Amasintha Temberero N’kukhala Dalitso
  • Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • Nkhani Yofanana
  • Utumiki wa Alevi
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • Zimene Tingaphunzire pa Zomwe Zinkachitika pa Msasa wa Aisiraeli
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • Yehova Amatsogolera Anthu Ake
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • N’chifukwa Chiyani Tiyenera Kupewa Mtima Wodandaula?
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
Onani Zambiri
Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
mwb21 March tsamba 12
Alongo awiri akulalikira kwa mayi amene akuchotsa zinyalala pakhomo pake pambuyo pa ngozi inayake ya m’chilengedwe.

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Yehova Amasintha Temberero N’kukhala Dalitso

Amowabu ankafuna kuchitira zoipa Aisiraeli (Nu 22:3-6)

Yehova anathandiza anthu ake (Nu 22:12, 34, 35; 23:11, 12)

Palibe amene angalimbane ndi Yehova (Nu 24:12, 13; bt 53 ¶5; it-2 291)

Vuto lililonse, ngakhalenso chizunzo, silingalepheretse kuti uthenga wabwino ulalikidwe mogwirizana ndi chifuniro cha Mulungu. Tikakumana ndi mavuto, kodi timadalira Atate wathu wakumwamba n’kumaonabe kuti kumulambira ndiye kofunika kwambiri?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena