Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb22 July tsamba 2
  • Barizilai Anali Wodzichepetsa

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Barizilai Anali Wodzichepetsa
  • Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
  • Nkhani Yofanana
  • Barizilai Anali Munthu Wodzichepetsa
    Nsanja ya Olonda—2007
  • Akhristu Achikulire, Yehova Amayamikira Kukhulupirika Kwanu
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2018
  • Kodi Tingatani Kuti Nthawi Zonse Tizikhala Odzichepetsa?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2017
  • Kudzichepetsa—Mkhalidwe Umene Umalimbikitsa Mtendere
    Nsanja ya Olonda—2000
Onani Zambiri
Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
mwb22 July tsamba 2
Barizilai akukana mwayi wa utumiki umene Mfumu Davide inamupatsa.

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Barizilai Anali Wodzichepetsa

Barizilai anapatsidwa mwayi wa utumiki ndi Mfumu Davide (2Sa 19:32, 33; w07 7/15 14 ¶5)

Chifukwa choti Barizilai anali wodzichepetsa, anakana mwayiwu mwaulemu (2Sa 19:34, 35; w07 7/15 14 ¶7)

Khalani odzichepetsa ngati Barizilai (w07 7/15 15 ¶1-2)

Kudzichepetsa kumatithandiza kudziwa zinthu zimene sitingakwanitse kuchita. Tiyenera kukhala odzichepetsa kuti tizisangalatsa Yehova. (Mik 6:8) Kodi kukhala ndi khalidwe limeneli kumatithandiza bwanji?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena