Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb22 November tsamba 13
  • Muzisangalala Mukamazunzidwa

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Muzisangalala Mukamazunzidwa
  • Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
  • Nkhani Yofanana
  • N’zotheka Kupirira Ena Akamakuzunzani
    Mungakhale Ndi Moyo Mpaka Kalekale—Kuphunzira Baibulo Mokambirana
  • Ozunzidwa Komabe Achimwemwe
    Nsanja ya Olonda—2004
  • Tisamaiwale Kupempherera Akhristu Amene Akuzunzidwa
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
  • Muzitsatira Mapazi a Khristu Mosamala Kwambiri
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
Onani Zambiri
Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2022
mwb22 November tsamba 13
Zithunzi za muvidiyo yakuti “Tikhoza Kumasangalalabe Ngakhale Kuti . . . Tikuzunzidwa.” M’bale Konstantin Bazhenov ali m’ndende. 1. Akuwerenga Baibulo. 2. Akupemphera. 3. Akuimba nyimbo za Ufumu mokweza mawu.

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

Muzisangalala Mukamazunzidwa

Akhristu amayembekezera kuti tsiku lina adzazunzidwa. (Yoh 15:20) Ngakhale kuti kuzunzidwa kumabweretsa nkhawa komanso nthawi zina n’kopweteka, n’zotheka kumasangalala uku tikupirira.​—Mt 5:10-12; 1Pe 2:19, 20.

ONERANI VIDIYO YAKUTI TIKHOZA KUMASANGALALABE NGAKHALE KUTI TIKUZUNZIDWA, KENAKO YANKHANI MAFUNSO OTSATIRAWA:

Kodi mwaphunzira chiyani kwa M’bale Bazhenov pa nkhani ya

  • kuwerenga Baibulo tsiku lililonse?

  • kulola kuti abale ndi alongo azikuthandizani?a

  • kupemphera pafupipafupi?

  • kuimba nyimbo za Ufumu?

  • kuuza ena zimene timakhulupirira?

a Tikhoza kumapempherera Akhristu omwe ali m’ndende ngakhalenso powatchula mayina. Koma n’zosatheka kuti ofesi ya nthambi izitumiza kwa Akhristuwa makalata omwe abale ndi alongo amawalembera.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena