Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb23 May tsamba 6
  • Yehova Amadalitsa Anthu Amene Amachita Zinthu Molimba Mtima

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Yehova Amadalitsa Anthu Amene Amachita Zinthu Molimba Mtima
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Nkhani Yofanana
  • N’chifukwa Chiyani Tiyenera Kuopa Yehova?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2023
  • Yehoyada Anali Wolimba Mtima
    Zimene Tingaphunzire Munkhani za M’Baibulo
  • Yoasi Anasiya Kutumikira Yehova Chifukwa Chocheza ndi Anthu Ochita Zoipa
    Nsanja ya Olonda—2009
  • Kutumikira Yehova Sikovuta Kwambiri
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
mwb23 May tsamba 6
Zithunzi: 1. Yehoyada ndi Yehosabati atenga Yehoasi yemwe anali wakhanda mozemba kuti akamubise. 2. Mkulu wa Ansembe Yehoyada akuveka chisoti Yehoasi kuti akhale mfumu.

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Yehova Amadalitsa Anthu Amene Amachita Zinthu Molimba Mtima

Yehosabati ndi mwamuna wake Yehoyada anateteza Yehoasi kwa Ataliya (2Mb 22:11, 12; w09 4/1 24 ¶1-2)

Yehoyada anachita zinthu molimba mtima kuti aike Yehoasi kukhala mfumu (2Mb 23:1-11, 14, 15; w09 4/1 24 ¶3-5)

Yehoyada analandira ulemu wapadera pamene anaikidwa m’manda limodzi ndi mafumu (2Mb 24:15, 16; it-1 379 ¶5)

FUNSO LOFUNIKA KULIGANIZIRA: Kodi ndi mbali ziti zimene ndiyenera kusonyeza kuti ndine wolimba mtima pa utumiki wanga?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena