Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb23 July tsamba 7
  • Kodi Mumagwira Ntchito Zonyozeka?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi Mumagwira Ntchito Zonyozeka?
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Mukukumbukira?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2019
  • Nehemiya Ankafuna Kutumikira, Osati Kutumikiridwa
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Muzitumikira Yehova Ndi Mtima Wonse
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • Muzikhalabe Wosangalala Ngakhale Pamene Zinthu Sizikuyenda Bwino
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
mwb23 July tsamba 7
Amuna ndi akazi a Chiisiraeli akugwira mwakhama ntchito yomanganso mpanda wa Yerusalemu.

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Kodi Mumagwira Ntchito Zonyozeka?

Mkulu wa ansembe ndi abale ake sanadzione kukhala anthu apamwamba kwambiri ndipo anagwira nawo ntchito yomanganso mpanda wa Yerusalemu (Ne 3:1)

Anthu ena otchuka “sanagonjere” kuti agwire nawo ntchitoyo (Ne 3:5; w06 2/1 10 ¶1)

Akazi okhulupirika anagwira nawo ntchitoyi yomwe inali yovuta komanso yofuna mphamvu zambiri (Ne 3:12; w19.10 23 ¶11)

Ntchito zambiri zimene zimachitika pampingo, zimafuna mphamvu kapena zimakhala zonyozeka komanso zina ena sangatione tikuzigwira.​—w04 8/1 18 ¶16.

DZIFUNSENI KUTI, ‘Kodi ndimamva bwanji ndikamagwira ntchito zoterezi, zomwe zimathandiza pa ntchito ya uthenga wabwino?’​—1Ak 9:23.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena