Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb23 November tsamba 11
  • Kukhulupirika Kumagwirizana ndi Zimene Timaganiza

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kukhulupirika Kumagwirizana ndi Zimene Timaganiza
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Nkhani Yofanana
  • Zosankha Zomwe Zimasonyeza Kuti Timadalira Yehova
    Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Mupeze Mayankho a Mafunso Awa
    Pulogalamu ya Msonkhano Wadera Wokhala ndi Woyang’anira Dera wa 2025-2026
  • Mupeze Mayankho a Mafunso Awa
    Pulogalamu ya Msonkhano Wadera Wokhala ndi Woimira Nthambi wa 2025-202
  • Zimene Inuyo Mwachita
    Kuwerenga Komanso Kuphunzitsa Mwaluso
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
mwb23 November tsamba 11
Mlongo akuyang’ana pawindo mosangalala.

MOYO WATHU WACHIKHRISTU

Kukhulupirika Kumagwirizana ndi Zimene Timaganiza

Timasonyeza kuti ndife okhulupirika, osati chifukwa cha zochita kapena zolankhula zathu zokha, koma chifukwa cha zimenenso timaganiza. (Sl 19:14) N’chifukwa chake Baibulo limatilimbikitsa kuti tiziganizira zinthu zilizonse zoona, zofunika kwambiri, zolungama, zoyera, zachikondi, zoyamikirika, khalidwe labwino lililonse, ndi chilichonse chotamandika. (Afi 4:8) N’zoona kuti nthawi zina sitingapeweretu kuganiza zinthu zoipa. Komabe kudziletsa kungatithandize kuti tichotse maganizo oipawo n’kuyamba kuganizira zinthu zabwino. Kukhalabe okhulupirika pa zimene timaganiza kungatithandize kuti tizichita zinthu mokhulupirika.—Mko 7:​21-23.

M’munsi mwa lemba lililonse, lembani maganizo amene muyenera kupewa:

Aro 12:3

Lu 12:15

Mt 5:28

Afi 3:13

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena