Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb23 November tsamba 14
  • Zimene Yobu Anachita Kuti Akhalebe Woyera

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zimene Yobu Anachita Kuti Akhalebe Woyera
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
  • Nkhani Yofanana
  • Mwamuna Wachitsanzo Chabwino Amene Anavomera Kum’langiza
    Nsanja ya Olonda—2000
  • “Yembekezera Yehova”
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2022
  • Musamaone Zinthu Zopanda Pake
    Kabuku ka Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2021
  • Yobu Analemekeza Dzina la Yehova
    Nsanja ya Olonda—2009
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu—2023
mwb23 November tsamba 14

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Zimene Yobu Anachita Kuti Akhalebe Woyera

Yobu anachita pangano ndi maso ake (Yob 31:1; w10 4/15 21 ¶8)

Yobu ankadziwa bwino mavuto amene angakhalepo chifukwa chochita zoipa (Yob 31:​2, 3; w08 9/1 11 ¶4)

Yobu ankakumbukira kuti Mulungu amaona zimene iye amachita (Yob 31:4; w10 11/15 5-6 ¶15-16)

M’bale akuyang’ana kumbali monyansidwa ndipo akutseka kompyuta yake mofulumira.

Kukhala woyera kumatanthauza kulankhula komanso kuchita zinthu zoyenera. Koma si zokhazi, timafunikanso kukhala oyera mumtima.—Mt 5:28.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena