-
Levitiko 27:7Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
7 Ndiyeno ngati zaka za munthu amene akuperekedwayo ndi zoyambira pa 60 kupita mʼtsogolo, akakhala wamwamuna, mtengo wake womwe unaikidwa ndi masekeli 15, ndipo akakhala wamkazi ndi masekeli 10.
-