Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Nehemiya 5:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Ndinauza anthu kuti tsiku lililonse azipha ngʼombe imodzi yamphongo, nkhosa zabwino kwambiri zokwana 6 ndiponso mbalame, ndipo pakatha masiku 10 tinkakhala ndi vinyo wambiri wamtundu uliwonse. Koma sindinapemphe kuti andipatse chakudya choyenera kuperekedwa kwa bwanamkubwa chifukwa anthuwa ankagwira kale ntchito yolemetsa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena