-
Nehemiya 5:18Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
18 Tsiku lililonse ndinali kuuza anthu kuti akonze ng’ombe imodzi yamphongo, nkhosa zosankhidwa mwapadera 6 ndi mbalame. Ndipo kamodzi pa masiku 10 alionse ndinali kupereka vinyo wochuluka wamtundu uliwonse.+ Kuwonjezera pamenepo, sindinapemphe kuti andipatse chakudya choyenera kuperekedwa kwa bwanamkubwa chifukwa utumiki umene anthuwa anali kuchita unali wolemetsa.
-