-
Danieli 9:27Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
27 Iye* adzasungira anthu ambiri pangano kwa mlungu umodzi. Ndiye pakatikati pa mlunguwo adzathetsa nsembe zanyama ndi nsembe zina zoperekedwa ngati mphatso.+
Wowonongayo adzabwera pamapiko a zinthu zonyansa ndipo zimene Mulungu wasankha zija zidzakhuthulidwanso pachowonongedwacho+ kufikira chitafafanizidwa.”
-