7 “Chotero Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena kuti, ‘Chifukwa chakuti anthu inu munali ovuta+ kuposa mitundu imene yakuzungulirani, ndipo simunayende m’malamulo anga, komanso simunatsatire zigamulo zanga,+ koma munatsatira zigamulo za mitundu imene yakuzungulirani,+