Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Nkosangalatsa kudziŵa kuti mtumwi Paulo wophunzira kwambiriyo anasankha kudzichirikiza mu utumiki mwa kupanga mahema, umisiri umene mwinamwake anauphunzira kwa atate wake. Kupanga mahema sikunali ntchito yosavuta. Nsalu ya ubweya wa mbuzi imene inagwiritsiridwa ntchito, yotchedwa cilicium, inali yokhuthala ndi ya nyankhalala, yovuta kudula ndi kusoka.—Machitidwe 18:1-3; 22:3; Afilipi 3:7, 8.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena