Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb18 May tsamba 5
  • Anaponya Zochuluka Kuposa Onse

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Anaponya Zochuluka Kuposa Onse
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
  • Nkhani Yofanana
  • Moyo wa Anthu Akale—Ndalama
    Nsanja ya Olonda—2011
  • Kodi Mukudziwa?
    Nsanja ya Olonda—2008
  • Chitsanzo Chabwino—Mkazi Wamasiye Wosauka
    Mayankho a Zimene Achinyamata Amafunsa, Buku Lachiwiri
  • Timakobidi Tiwiri Tochepa Mphamvu
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2012
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2018
mwb18 May tsamba 5
Mayi wamasiye akuponya ndalama moponyamo zopereka

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | MALIKO 11-12

Anaponya Zochuluka Kuposa Onse

12:41-44

Kodi mavesiwa akutithandiza bwanji kumvetsa mfundo zotsatirazi?

  • Yehova amayamikira zimene timachita

  • Tizitumikira Yehova ndi mtima wonse

  • Tisamayerekezere zomwe tikuchita ndi zimene anthu ena akuchita kapenanso ndi zimene tinkachita m’mbuyomu

  • Nawonso osauka akhoza kupereka ngakhale tindalama tochepa tomwe angakhale nato

Kodi ndi zinthu zinanso ziti zimene mwaphunzira m’nkhaniyi?

KODI MUKUDZIWA?

Maleputoni awiri

Leputoni

Zikuoneka kuti tindalama timene mayi wamasiye uja anaponya moponyamo zopereka tinali timaleputoni tiwiri. Munthu ankapatsidwa timaleputoni tiwiri akagwira ntchito kwa 15 minitsi. Yesu anasonyeza kuti tingaphunzire zambiri kuchokera kwa mayi wamasiyeyu amene anapereka timakobidi tiwiri tating’ono.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena