Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Chikristu Chifalikira Kumayiko Ena
    ‘Onani Dziko Lokoma’
    • Patangopita nthaŵi yochepa Yesu atanena mawu ameneŵa, Phwando la Pentekoste linasonkhanitsa Ayuda ndi anthu oloŵa Chiyuda ochokera m’madera onse a Ufumu wa Roma, osonyezedwa pamapu ali m’munsiŵa. Chikristu chinafalikira kwambiri pamene mtumwi Petro analalikira kwa anthuwo tsiku limenelo.—Mac. 2:9-11.

  • Chikristu Chifalikira Kumayiko Ena
    ‘Onani Dziko Lokoma’
    • [Bokosi patsamba 32]

      ANACHOKERA KU . . .

      Ayuda ndi oloŵa Chiyuda omwe anamva uthenga wabwino pa Pentekoste 33 C.E. anachokera ku Aparti, Mediya, Elamu, Mesopotamiya, Yudeya, Kapadokiya, Ponto, Asiya, Frugiya, Pamfuliya, Igupto, Libiya, Roma, Kurene, ndi Arabiya. Ambiri anabatizidwa. Kodi mukuganiza kuti anakachita chiyani atabwerera kwawo?

  • Chikristu Chifalikira Kumayiko Ena
    ‘Onani Dziko Lokoma’
    • C2 KRETE

  • Chikristu Chifalikira Kumayiko Ena
    ‘Onani Dziko Lokoma’
    • F4 ARABIYA

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena