Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 47
  • Muzipemphera kwa Yehova Nthawi Zonse

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Muzipemphera kwa Yehova Nthawi Zonse
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Muzipemphera kwa Yehova Tsiku Lililonse
    Imbirani Yehova
  • Pempherani kwa Yehova Tsiku ndi Tsiku
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Kuyandikira kwa Mulungu m’Pemphero
    Kodi Mulungu Amafunanji kwa Ife?
  • Yesu Atiphunzitsa Ife Kupemphera
    Kumamumvetsera Mphunzitsi Wamkuru’yo
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 47

NYIMBO 47

‘Muzipemphera kwa Yehova Nthawi Zonse’

Losindikizidwa

(1 Atesalonika 5:17)

  1. 1. Pemphera kwa Yehova amamva.

    Ndi mwayi umene wakupatsa.

    Umuuze zamumtima mwako,

    Ndi wodalirika, bwenzi lako.

    Pemphera kwa Yehova.

  2. 2. Pemphera kwa Yehova thokoza.

    Upemphe akukhululukire.

    Umuuze zomwe walakwitsa,

    Amadziwa zofooka zako.

    Pemphera kwa Yehova.

  3. 3. Pemphera kwa Yehova m’mavuto,

    Ndi M’lungu wako akuthandiza.

    Upemphe kuti akuteteze,

    Mukhulupirire usaope.

    Pemphera kwa Yehova.

(Onaninso Sal. 65:5; Mat. 6:​9-13; 26:41; Luka 18:1.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena