Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 174
  • Dzukani, Chirimikani, Khalani Wamphamvu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Dzukani, Chirimikani, Khalani Wamphamvu
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Khalani Maso, Limbani, Khalani Amphamvu
    Imbirani Yehova
  • Khala Maso, Khala Wolimba, Khala Wamphamvu
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • “Lupanga la Yehova ndi la Gideoni”
    Nsanja ya Olonda—2005
  • Gideon ndi Amuna Ake 300
    Bukhu Langa la Nkhani za Baibulo
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 174

Nyimbo 174

Dzukani, Chirimikani, Khalani Wamphamvu

(1 Akorinto 16:13)

1. Dzukani, muchirimike

Munkhondo yoyenera.

Chitanitu mwachamuna,

Chilakiko chafika.

Pansi pa Gideoni ’Mkulu,

Tazinga msasa wa Midyani.

Mfu’ yankhondo iperekedwa,

Kupirikitsa mdani.

2. Dzukani, mukhale maso,

Achire mukumvera.

Yense alabadiretu

Zomwe Yesu anena.

Mwachitsanzo chake tidziŵa

Kupeza chiyanjo cha M’lungu.

Monga gulu titumikire,

Mokhulupirikabe.

3. Dzukani, ndi kupilira;

Yembekezani pa Ya.

Alamula zinthu zonse;

Sadzachita mochedwa.

Monga ’muna a Gideoni,

Mkuluyo adzatilamula.

Potero mverani lamulo.

Lidzatamanda dzina.

4. Dzukani, mugwirizane

Potchinjiriza mbiri.

M’njira ya teokratiki

Njofunika kwambiri.

Tifuule ndi anthu a Ya:

“Lupanga la Ya n’Gideoni!”

Dzukani m’chirimike m’khondo!

Kufikira mapeto!

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena