Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 155
  • ‘Landiranani’!

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • ‘Landiranani’!
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Tizilandilana
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Landiranani
    Imbirani Yehova
  • Kulandira Mfumu Yakudzayo!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Tizichita Zinthu Zogwirizana Ndi Dzina Lathu
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 155

Nyimbo 155

‘Landiranani’!

(Aroma 15:7)

1. O landiranani monga anachita Kristu!

Poti Kristu anafera mbale m’landireni.

Chotero amphamvu athandize ofooka,

Kuwathandiza kuteteza chiyembekezo.

Zinthu zolembedwa ndi aneneri akale

Zingathe kukulitsa chiyembekezo chathu.

Chotero tisadzikondweretse ife tokha,

Koma kuwona zokonda zawo monga zathu.

2. Ya akusonkhanitsa anthu osamenyana.

Nthaŵi yadzera Mwana’ke kudzetsa mtendere.

Akutenga anthu m’mitundu ndi malirime,

M’mitima mwawo muli kukonda malamulo.

Polemekeza M’lungu tilandirabe ena

Timayanjana ndi onse popanda kusankha.

Ndimwaŵi waukulu kutsanzira Mulungu.

Monga otsanza Mwanayo, tikuze mitima.

3. Tilimbikitse anthu kutamanda Yehova,

Kukondwa ndi mtundu wake, ndi kumutamanda.

Tilengezebe panyumba ndi pamakwalala,

Mbiri yake ndi dzina kwa okumana nawo.

Ulemuwu wa kutamanda Ya sudzadzanso.

Ndiwo masiku otsiriza kwa olungama.

Tikonde abale M’lungu akhale wowona;

Inde mulandiranedi Mawuwo atero.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena