Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 12
  • “Mulungu Akonda Wopereka Mokondwera”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Mulungu Akonda Wopereka Mokondwera”
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • “Mulungu Amakonda Munthu Wopereka Mokondwera”
    Nsanja ya Olonda—2013
  • Yehova Amakonda Opatsa Mokondwerera
    Nsanja ya Olonda—1992
  • Kodi Baibulo Limanena Zotani pa Nkhani ya Kupatsa?
    Kuyankha Mafunso a M’Baibulo
  • Tsanzirani Mulungu Wathu Wachisangalalo, Yehova
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2006
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 12

Nyimbo 12

“Mulungu Akonda Wopereka Mokondwera”

(2 Akorinto 9:7)

1. Potumikira Tate, tiyenera kudziŵa

Kuti ngwokoma mtima ndi wachikondi.

Poti ali Wopatsa; anapatsa Mwana’ke,

Nafuna kuwonjola mitundu yonseyo.

2. Tingachite bwinodi kumtsanzira mkupatsa.

Tikapatsa mokondwa, tidzakondwera.

Nthaŵi yathu ndi chuma ziridi za Yehova.

Tikamupatsa iye, sitidzalakwanso.

3. Kupatsa mwachimwemwe kukondwetsa Yehova.

Kukonza chiphunzitso ndi chikondinso.

Nkofunika kwambiri kukachoka mumtima;

Kudzadzetsa chimwemwe ndi chisangalalo.

4. Motero Tiyamika M’lungu ndi Kristu Yesu,

Pokuza kulambira kwathu kowona.

Mtima utisonkheze tipereke mokondwa

Ndi kukondweretsa Ya pokhala ndi moyo.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena