Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 214
  • Kulondola Njira ya Mulungu ya Moyo

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kulondola Njira ya Mulungu ya Moyo
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • ‘Kondwerani mwa Yehova’
    Nsanja ya Olonda—2003
  • Kugwirizana pa Kulambira Masiku Athu Ano—Kodi Kumatanthauzanji?
    Lambirani Mulungu Woona Yekha
  • Mulungu Imvani Pemphero Langa
    Imbirani Yehova
  • Munapereka Mwana Wanu Wobadwa Yekha
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 214

Nyimbo 214

Kulondola Njira ya Mulungu ya Moyo

(Miyambo 9:10, 11)

1. Moyo mphatso ya mtengo wapatali,

Mwa Kristuyo! Tiusamalire.

Tivomereza, kwa inu Yehova:

Njira yanu itisangalatsa.

2. Moyenelera tiwopa inu Ya.

Tipeza chidziŵitso ndi nzeru.

Mulamulo lanu tisangalala;

Tiyenda nalo mwa umulungu.

3. Moyo ngwachifuno ndinu wabwino.

Mwa Mwana’nu taphunzira moyo.

Musakonde dziko ndi zinthu zake.

Mufunefune chisangalalo.

4. Tithandizeni kuphunzitsa moyo,

Popeza Ufumu wayandika.

Tilalikire kwa ofatsa m’dziko,

Mubwezeretsa kulambirako.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena