Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ssb nyimbo 186
  • Chimwemwe Chathu Chaumulungu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Chimwemwe Chathu Chaumulungu
  • Imbirani Yehova Zitamando
  • Nkhani Yofanana
  • Chimwemwe Ndi Khalidwe Limene Mulungu Amapereka
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2018
  • Tumikirani Yehova ndi Chimwemwe cha Mtima
    Nsanja ya Olonda—1995
  • Kutumikira Yehova Mwachimwemwe
    Nsanja ya Olonda—1991
  • Chimwemwe cha Yehova Ndicho Linga Lathu
    Nsanja ya Olonda—1995
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Zitamando
Ssb nyimbo 186

Nyimbo 186

Chimwemwe Chathu Chaumulungu

(Afilipi 4:4)

1. Tifunikira chimwemwe

Kuti tipilire.

Chimwemwechi chimafuna

Chikhulupiliro.

Simkhalidwe wakanthaŵi;

Ndiwanthaŵi zonse.

Nchifukwa timaŵerenga

Kuti “Kondwerani!”

2. Tikondwere kuti ndife

Odziŵa Mulungu;

Tiri ndi ulemu monga

Mboni muumodzi.

Tikondwa chifukwa M’lungu

Adzatamandidwa,

Akufawo adzauka

Nadzakhala m’dziko.

3. Kukulitsa chimwemwechi

Timvere Mulungu,

Titchinjirize mitima

Kupanda njirunso.

Tikhale amasobe ndi

Kutamanda M’lungu;

Nthaŵi zonse tiganize

Pazopindulitsa.

4. Nkana tiponderezedwa

Tipeza zambiri,

Chimwemwe ndi mphotho yathu

Pomtumikiradi.

Tiri mboni za Yehova

Kunena za iye.

Tidzazidwe ndi chimwemwe

Pamodzi ndi ena.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena