Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 10
  • “Ine Ndilipo! Nditumizeni”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Ine Ndilipo! Nditumizeni”
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • “Ine Ndilipo! Nditumizeni”
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • “Ndine Pano! Munditumize Ine”
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Tidzakhala Ndi Moyo Wosatha
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Kukonzekera Kupita Kokalalikira
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 10

Nyimbo 10

“Ine Ndilipo! Nditumizeni”

Losindikizidwa

(Yesaya 6:8)

1. Lero anthu akunyoza

Dzina labwino la M’lungu.

Ena am’yesa wankhanza,

Nati: “Kulibe Mulungu.”

Ndani adzaliyeretsa

Dzina la Mulungu wathu?

“Ndilipo nditumizeni.

Ndidzaimbira nokhanu

(KOLASI)

Sindingachitirenso mwina.

Nditumizeni Mbuye.”

2. Anthu akutonza M’lungu

Ndikumati ndi wochedwa.

N’kumalambira mafano

Ena eti Kaisara.

Ndani adzawachenjeza

Za nkhondo yomalizayo?

“Ndilipo nditumizeni.

Ndidzachenjeza oipa.

(KOLASI)

Sindingachitirenso mwina.

Nditumizeni Mbuye.”

3. Anthu ofatsa ’kulira,

Zoipa zikuchuluka.

Iwo akufunafuna

Choonadi chomasula.

Ndani adzawatonthoza?

Ndani adzawathandiza?

“Ndilipo, nditumizeni.

Ndidzaphunzitsa ofatsa.

(KOLASI)

Sindingachitirenso mwina.

Nditumizeni Mbuye.”

(Onaninso Sal. 10:4; Ezek. 9:4.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena