Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 80
  • Tizichita Zinthu Zabwino

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tizichita Zinthu Zabwino
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Khalidwe la Ubwino
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Mbali Yodabwitsa ya Ubwino wa Mulungu
    Nsanja ya Olonda—1989
  • Ubwino​—Kodi Tingatani Kuti Tikhale ndi Khalidweli?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2019
  • Tsanzirani Ubwino wa Yehova
    Utumiki Wathu wa Ufumu—2003
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 80

Nyimbo 80

Tizichita Zinthu Zabwino

Losindikizidwa

(Salimo 119:66)

1. N’zosangalatsa kudziwa

Ubwino wa Yehova.

Monga Tate wakumwamba

Amachita zabwino.

Amasonyeza chifundo

Ndipo amatikonda.

N’ngoyenera kum’lambira

Ndi kumutumikira.

2. M’chifaniziro cha M’lungu

Anatilenga ife,

Kuti makhalidwe ake

Inde, tiwasonyeze.

Ubwino wathu ukule

Mulungu tim’tsanzire,

Chipatso cha mzimu wake

Tifuna tisonyeze.

3. Makamaka ’bale athu

Tiwakomere mtima,

Komanso kwa anthu onse

Tisonyeze ubwino.

Pomwe tikulalikira

Uthenga wa Ufumu

Tikhale opanda tsankho

Abwino m’zinthu zonse.

(Onaninso Sal. 103:10; Maliko 10:18; Agal. 5:22; Aef. 5:9.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena