Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sn nyimbo 85
  • Mphoto Yaikulu Yochokera Kwa Yehova

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mphoto Yaikulu Yochokera Kwa Yehova
  • Imbirani Yehova
  • Nkhani Yofanana
  • Yehova “Akulipire Mokwanira”
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Kuchirikiza Nyumba ya Mulungu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Kutumikira Yehova Ndi Moyo Wonse
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Lambirani Yehova Muli Achinyamata
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova
sn nyimbo 85

Nyimbo 85

Mphoto Yaikulu Yochokera Kwa Yehova

Losindikizidwa

(Mateyu 19:29)

1. Yehova amadziwa anthu onse

Omwe amam’tumikira.

Amadziwa kuti pa nthawi zina

Zinthu zina ’mamanidwa.

Ngati mwasiya abale ndi nyumba

M’lungu akudziwa bwino.

Amatipatsa ’bale auzimu

Ndi moyo m’paradaiso.

(KOLASI)

Yehova wotonthoza aone

Ndiponso akupatseni mphoto.

Bisalani m’mapiko ake,

N’ngokhulupirika, Iye n’ngwabwino.

2. Mwina n’kusankha kwawo mwina ayi

Kuti ena sali m’banja.

Akamafuna Ufumu wa M’lungu

Iwo amadalitsidwa.

Amasungulumwatu nthawi zina,

Zimenezi tikudziwa.

Monga abale ndi alongo awo

Tikhale olimbikitsa.

(KOLASI)

Yehova wotonthoza aone

Ndiponso akupatseni mphoto.

Bisalani m’mapiko ake,

N’ngokhulupirika, Iye n’ngwabwino.

(Onaninso Ower. 11:38-40; Rute 2:12; Mat. 19:12.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena