Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb16 November tsamba 4
  • Muzisangalala Chifukwa Chogwira Ntchito Mwakhama

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Muzisangalala Chifukwa Chogwira Ntchito Mwakhama
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
  • Nkhani Yofanana
  • Sangalalani Chifukwa Chogwira Ntchito Mwakhama
    Kodi Mungatani Kuti ‘Mulungu Apitirize Kukukondani’?
  • Muzisangalala Ndi Ntchito Yanu
    Kodi Mungatani Kuti Mulungu Azikukondani?
  • Kodi Mungatani Kuti Muzisangalala Ndi Ntchito Yanu?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • Sonyezani Mtima wa Kristu
    Nsanja ya Olonda—2000
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
mwb16 November tsamba 4

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | MLALIKI 1-6

Muzisangalala Chifukwa Chogwira Ntchito Mwakhama

Yehova amafuna kuti tizisangalala ndi ntchito yathu ndipo amatiphunzitsa mmene tingachitire zimenezi. Munthu akhoza kumasangalala ndi ntchito yake ngati amaigwira ndi maganizo oyenera.

Mukhoza kumasangalala ndi ntchito yanu . . .

3:13; 4:6

  • Munthu akusangalala ndi ntchito yake

    mukamaona ntchitoyo moyenera

  • Munthu akuganizira mmene ntchito yake imathandizira anthu ena

    mukamaganizira mmene ntchitoyo imathandizira anthu ena

  • Munthu akudyera limodzi ndi banja lake

    mukamaigwira mwakhama, komabe mukaweruka muziyesetsa kuika maganizo pa banja lanu ndiponso kutumikira Yehova

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena