Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 138
  • Imvi Ndi Chisoti cha Ulemerero

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Imvi Ndi Chisoti cha Ulemerero
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Ulemerero Umene Umabwera Chifukwa cha Imvi
    Imbirani Yehova
  • Imvani Pemphero Langa
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Mulungu Imvani Pemphero Langa
    Imbirani Yehova
  • Yehova, Nyonga Yathu ndi Mphamvu Yathu
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 138

NYIMBO 138

Imvi Ndi Chisoti cha Ulemerero

Losindikizidwa

(Miyambo 16:31)

  1. 1. Pano tili ndi anthu

    Achikulire.

    Akukondabe M’lungu

    Sanamusiye.

    Ena akuvutika

    Ndi umasiye.

    M’lungu atonthozeni,

    Alimbitseni.

    (KOLASI)

    Mumakumbukira

    Zochita zawo.

    M’lungu auzeni:

    “Mwachita bwino.”

  2. 2. Imvi za olungama

    Ndi zokongola.

    Yehova M’lungu wathu

    Amawakonda.

    Tikumbukire kuti

    Kale kalelo,

    Pa unyamata wawo

    Ankayesetsa.

    (KOLASI)

    Mumakumbukira

    Zochita zawo.

    M’lungu auzeni:

    “Mwachita bwino.”

(Onaninso Sal. 71:​9, 18; Miy. 20:29; Mat. 25:​21, 23; Luka 22:28; 1 Tim. 5:1.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena