Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb19 February tsamba 5
  • Kodi ‘Mukudikira Mwachidwi’?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi ‘Mukudikira Mwachidwi’?
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Nkhani Yofanana
  • “Kuyembekezera Mwachidwi”
    Nsanja ya Olonda—1998
  • Tizisangalala ndi Chiyembekezo Chathu
    Nsanja ya Olonda—2012
  • Ufulu Waulemerero Posachedwapa kwa Ana a Mulungu
    Nsanja ya Olonda—1998
  • Tiziyembekezerabe
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
Onani Zambiri
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
mwb19 February tsamba 5

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | AROMA 7-8

Kodi ‘Mukudikira Mwachidwi’?

8:19-21

  • “Chilengedwe”: anthu amene akuyembekezera kudzakhala padziko lapansi

  • ‘Ulemelero wa ana a Mulungu udzaonekera’: pamene odzozedwa adzathandiza Yesu kuwononga dziko loipa la Satanali

  • “Maziko a chiyembekezo”: zimene Yehova akulonjeza kuti adzatipulumutsa kudzera mu imfa komanso kuukitsidwa kwa Yesu

  • ‘Kumasulidwa ku ukapolo wa kuvunda’: anthu adzayamba kumasulidwa pang’onopang’ono kuchokera ku mavuto amene amabwera chifukwa cha uchimo ndi imfa

M’bale wachinyamata akuphunzira Baibulo payekha, akupereka ndemanga pamisonkhano, akukana pamene mtsikana wina akumunyengerera, akusangalala ndi macheza abwino

Kodi mungasonyeze bwanji kuti ‘mukudikira mwachidwi nthawi imene ulemelero wa ana a Mulungu udzaonekere’?

  • Muziphunzira Baibulo mwakhama komanso muzipempha Mulungu kuti akupatseni mzimu wake

  • Muzigwiritsa ntchito chilichonse chimene Yehova amatipatsa kuti tikhale naye paubwenzi

  • Musalole kuti Satana akupusitseni ndi mfundo yakuti malamulo a Mulungu ndi opanikiza

  • Muzigwiritsa ntchito zimene mumaphunzira pa moyo wanu

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena