Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • mwb19 February tsamba 6
  • Fanizo la Mtengo wa Maolivi

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Fanizo la Mtengo wa Maolivi
  • Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
  • Nkhani Yofanana
  • ‘Nzeru za Mulungu N’zozama’ Kwambiri
    Nsanja ya Olonda—2011
  • Mtengo Wauŵisi wa Azitona M’nyumba ya Mulungu
    Nsanja ya Olonda—2000
  • Tizikhulupirira Kwambiri Ufumu wa Mulungu
    Nsanja ya Olonda—2014
  • Yobu Sankakayikira Kuti Akufa Adzauka
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2016
Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2019
mwb19 February tsamba 6

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | AROMA 9-11

Fanizo la Mtengo wa Maolivi

11:16-26

Kodi mbali zosiyanasiyana za mtengo wa maolivi wotchulidwa m’mavesiwa zimaimira chiyani?

Mtengo wa maolivi wotchulidwa mu chaputala 11 cha buku la Aroma
  • Mtengo: kukwaniritsidwa kwa cholinga cha Mulungu chokhudza pangano la Abulahamu

  • Thunthu: Yesu, yemwe ndi mbali yoyambirira ya mbewu ya Abulahamu

  • Nthambi: chiwerengero chokwanira cha mbali yachiwiri ya mbewu ya Abulahamu

  • Nthambi zomwe “zinadulidwa”: mtundu wa Isiraeli womwe unakana Yesu

  • Nthambi zomwe ‘zinalumikizidwa’: Akhristu odzozedwa ochokera m’mitundu yonse

Monga mmene ulosi umanenera, mbewu ya Abulahamu yomwe ndi Yesu komanso Akhristu odzozedwa okwana 144,000, idzabweretsa madalitso “kwa anthu a mitundu ina.”​—Aroma 11:12; Gen. 22:18

Kodi ndikuphunzira zotani zokhudza Yehova pa nkhani ya mmene anakwaniritsira cholinga chake chonena za mbewu ya Abulahamu?

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena