Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 30
  • Atate Wanga, Mulungu Wanga Ndiponso Bwenzi Langa

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Atate Wanga, Mulungu Wanga Ndiponso Bwenzi Langa
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Atate Wanga, Mulungu Wanga Ndiponso Bwenzi Langa
    Imbirani Yehova
  • Moyo Wopanda Mapeto—Potsiriza!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • ‘Dzina Lanu Ndi Yehova’
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Athandizeni Kukhala Olimba
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 30

NYIMBO 30

Atate Wanga, Mulungu Wanga Ndiponso Bwenzi Langa

Losindikizidwa

(Aheberi 6:10)

  1. 1. Nthawi zina m’dzikoli

    Zinthu zingakhale zovuta.

    Komabe ndizingoti

    Moyo ndi wabwino.

    (KOLASI)

    M’lungu ndi wolungama

    Sadzaiwala ntchito zanga.

    Ali pafupi nane

    Nthawi zonse sanditaya.

    Iye adzandipatsa

    Zonse zomwe ndifunikira.

    Ndi Atate, Ndi Mulungu,

    Bwenzi langa.

  2. 2. Panopa ndakalamba.

    Tsopano ndi nthawi yovuta

    Koma chiyembekezo

    Changa ndi champhamvu.

    (KOLASI)

    M’lungu ndi wolungama

    Sadzaiwala ntchito zanga.

    Ali pafupi nane

    Nthawi zonse sanditaya.

    Iye adzandipatsa

    Zonse zomwe ndifunikira.

    Ndi Atate, Ndi Mulungu,

    Bwenzi langa.

(Onaninso Sal. 71:​17, 18.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena