Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 128
  • Tipirire Mpaka Mapeto

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tipirire Mpaka Mapeto
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Pirirani Mpaka pa Mapeto
    Imbirani Yehova
  • Tipitirizebe Kupirira
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Tipirirabe Mpaka Mapeto
    Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Pitirizanibe Kukhala M’gulu la Yehova
    Gulu Lochita Chifuniro cha Mulungu
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 128

NYIMBO 128

Tipirire Mpaka Mapeto

Losindikizidwa

(Mateyu 24:13)

  1. 1. Mawu a Mulungu wathu

    Amalimbikitsa.

    Zinthu zomwe waphunzira

    Zonse ndi zolondola.

    Uzikhulupirikabe

    Podikira mapeto.

    Usaope mayesero

    Udzakhala wolimba.

  2. 2. Chikondi chako kwa M’lungu

    Chisachepe mphamvu.

    Upirirebe ngakhale

    Mayesero akule.

    Kaya akhale otani

    Usamachite mantha.

    Yehova Mulungu wako

    Adzakupulumutsa.

  3. 3. Yemwe angapirirebe

    Adzapulumuka.

    Mayina akulembedwa

    Mubuku la moyotu.

    Lola kuti kupirira

    Kugwire ntchito yake.

    Yehova adzachititsa

    Kuti usangalale.

(Onaninso Aheb. 6:19; Yak. 1:4; 2 Pet. 3:12; Chiv. 2:4.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena