Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 160
  • “Uthenga Wabwino”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Uthenga Wabwino”
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Tilalikire Mbiri Yabwino Imeneyi Yaufumu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Kufalitsa “Uthenga Wabwino wa Zinthu Zabwino”
    Nsanja ya Olonda—2005
  • Lalikirani “Mbiri Yabwino Imeneyi Yaufumu”!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Kodi Uthenga Wabwino Ungakupindulitseni Motani?
    Nsanja ya Olonda—1992
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 160

NYIMBO 160

“Uthenga Wabwino”

Losindikizidwa

(Luka 2:10)

  1. 1. Tilemekeze M’lungu

    Amatikonda.

    Anatumiza Mwana wake

    Kudzatipatsa

    Chiyembekezochi.

    (KOLASI)

    Uthengawu ndi

    Wosangalatsa.

    Ndi wabwinodi.

    Tilalikire

    Za uthengawu.

    Khristu wabadwa,

    Mpulumutsi wathu.

  2. 2. Azidzalamulira

    Mwachilungamo.

    Abweretsa Paradaiso

    Ndipo Ufumu

    Wakewo sudzatha.

    (KOLASI

    Uthengawu ndi

    Wosangalatsa.

    Ndi wabwinodi.

    Tilalikire

    Za uthengawu.

    Khristu wabadwa,

    Mpulumutsi wathu.

    (KOLASI)

    Uthengawu ndi

    Wosangalatsa.

    Ndi wabwinodi.

    Tilalikire

    Za uthengawu.

    Khristu wabadwa,

    Mpulumutsi wathu.

(Onaninso Mat. 24:14; Yoh. 8:12; 14:6; Yes. 32:1; 61:2.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena