Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 24
  • Bwerani Kuphiri la Yehova

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Bwerani Kuphiri la Yehova
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Bwerani Kuphiri la Yehova
    Imbirani Yehova
  • “Lalikira Mawu”
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Tizilalikira Anthu a Mitundu Yonse
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Tizilalikira kwa Anthu a Mitundu Yonse
    Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 24

NYIMBO 24

Bwerani Kuphiri la Yehova

Losindikizidwa

(Yesaya 2:​2-4)

  1. 1. Phiri la Yehova

    Tangoliyang’anani.

    Lakwezedwa pamwamba

    Pa mapiri onse.

    Anthu akubwera

    Kuchokera kutali.

    Akuitanizana

    Bwerani kwa M’lungu.

    Tsopano wochepa

    Wasanduka mtundu wamphamvu.

    Tikuona kuti

    Tikudalitsidwa ndi M’lungu.

    Ambiri tsopano

    Akuvomerezadi

    Ulamuliro wake

    Mokhulupirika.

  2. 2. Yesu walamula

    Kuti tipite konse

    Tikalalikire

    Uthenga wa Ufumu.

    Khristu wayambano

    Ulamuliro wake

    Ndipo akuti tikhale

    Kumbali yake.

    Ndi zosangalatsa

    Kuona khamu lalikulu

    Likukulirabe

    Ndipo tonse tikuthandiza.

    Tonse tifuule

    Tiziitana anthu.

    ‘Bwerani kuphiri

    La Yehova Mulungu.’

(Onaninso Sal. 43:3; 99:9; Yes. 60:22; Mac. 16:5.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena