Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 85
  • Tizilandilana

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Tizilandilana
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Landiranani
    Imbirani Yehova
  • ‘Landiranani’!
    Imbirani Yehova Zitamando
  • Achititseni Kudzimva Olandiridwa pa Chikumbutso
    Utumiki Wathu wa Ufumu—1994
  • Kulandira Mfumu Yakudzayo!
    Imbirani Yehova Zitamando
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 85

NYIMBO 85

Tizilandirana

Losindikizidwa

(Aroma 15:7)

  1. 1. Takulandirani inu nonse.

    Mwasonkhana kudzaphunzira

    Choonadi chochoka kwa M’lungu.

    Iye akaitana timavomera.

  2. 2. Tikuyamikira abalewa

    Chifukwa amatilandira.

    Tiziwasonyezatu chikondi.

    Tilandirenso ena odzasonkhana.

  3. 3. Aliyense akuitanidwa

    Kuti apeze choonadi.

    M’lungu watikokera kwa iye

    Choncho tilandirane ndi mtima wonse.

(Onaninso Yoh. 6:44; Afil. 2:29; Chiv. 22:17.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena