Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 87
  • Bwerani Mudzalimbikitsidwe

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Bwerani Mudzalimbikitsidwe
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Bwerani Mudzatsitsimulidwe!
    Imbirani Yehova
  • Kukonzekera Kupita Kokalalikira
    Imbirani Yehova Mosangalala
  • Kukonzekera Kupita Kolalikira
    Imbirani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Lambirani Yehova Muli Achinyamata
    Imbirani Yehova
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 87

NYIMBO 87

Bwerani Mudzalimbikitsidwe

Losindikizidwa

(Aheberi 10:​24, 25)

  1. 1. Tili mu dziko lomwe ndi loipa,

    Anthu sakudziwa M’lungu.

    Choncho tikufunika malangizo

    Oti atitsogolere.

    Misonkhano yathu imathandiza

    Kukhala osangalala.

    Timamvako mawu olimbikitsa

    Cholinga tisafooke.

    Sitidzasiya kugwiritsa ntchito

    Malamulo a Yehova.

    Pamisonkhano timalangizidwa

    Kumakonda choonadi.

  2. 2. Yehova amadziwa bwino zinthu

    Zomwe timafunikira.

    Tikamasonkhana timasonyeza

    Kuti timamudalira.

    Malangizo ochoka kwa akulu

    Amakhala othandiza.

    Timadziwa kuti sitili tokha

    Abale amathandiza.

    Choncho poyembekezera m’tsogolo

    Tisasiye kusonkhana.

    Tiziphunzira kugwiritsa ntchito

    Mawu a Mulungu wathu.

(Onaninso Sal. 37:18; 140:1; Miy. 18:1; Aef. 5:16; Yak. 3:17.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena