Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 134
  • Ana Ndi Mphatso Yochokera kwa Mulungu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Ana Ndi Mphatso Yochokera kwa Mulungu
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Ana Ndi Mphatso Yochokera kwa Mulungu
    Imbirani Yehova
  • Muzikhulupirira Abale Anu
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzira)—2022
  • Kukhulupirira Ena N’kofunika Kwambiri Kuti Munthu Akhale Wosangalala
    Nsanja ya Olonda—2003
  • Abusa Ndi Mphatso
    Imbirani Yehova Mosangalala
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 134

NYIMBO 134

Ana Ndi Mphatso Yochokera Kwa Mulungu

Losindikizidwa

(Salimo 127:​3-5)

  1. 1. Mwamuna ndi mkazi wake

    Akalandira mphatso ya mwana,

    Ayenera kukumbukira

    Mwanayo si wawo okha.

    Ndi mphatso yochoka kwa M’lungu.

    Amapatsa chikondi ndi moyo.

    Amapereka malangizo

    Othandizadi kwa makolo.

    (KOLASI)

    Mphatsoyi ndi yopatulika

    Ndipo muisamalire.

    Muphunzitseni choonadi

    Ndipo mudzamuthandiza.

  2. 2. Mawu onse a Mulungu

    Azikhalatu mumtima mwanu.

    Muziuzanso ana anu,

    Uwu ndi udindo wanu.

    Muziwaphunzitsa poyenda,

    Podzuka ndi pa nthawi yopuma.

    Akamakula saiwala.

    Azilandira madalitso.

    (KOLASI)

    Mphatsoyi ndi yopatulika

    Ndipo muisamalire.

    Muphunzitseni choonadi

    Ndipo mudzamuthandiza.

(Onaninso Deut. 6:​6, 7; Aef. 6:4; 1 Tim. 4:16.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena