Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 45
  • “Zimene Ndimaganizira Mozama”

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • “Zimene Ndimaganizira Mozama”
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Kusinkhasinkha kwa Mtima Wanga
    Imbirani Yehova
  • Kusinkhasinkha Kumene Kumapindulitsa
    Galamukani!—2000
  • Kusinkhasinkha
    Galamukani!—2014
  • Tiziganizira Kwambiri za Yehova
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 45

NYIMBO 45

“Zimene Ndimaganizira Mozama”

Losindikizidwa

(Salimo 19:14)

  1. 1. Zomwe ndimaganizira

    Mozama mumtima mwanga,

    Zizikusangalatsani

    Kuti ndikhale wolimba.

    Pamene ndili ndi nkhawa

    N’kumalephera kugona,

    Ndiganizire mozama

    Zinthu zondilimbikitsa.

  2. 2. Zilizonse zolungama,

    Zofunika ndi zoona,

    Ndikamaziganizira

    Zizindipatsa mtendere.

    Nzeru zanu n’zofunika

    Komanso ndi zochuluka,

    Choncho ndiziganizira

    Zonena zanu mozama.

(Onaninso Sal. 49:3; 63:6; 139:​17, 23; Afil. 4:​7, 8; 1 Tim. 4:15.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena