Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 126
  • Khala Maso, Khala Wolimba, Khala Wamphamvu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Khala Maso, Khala Wolimba, Khala Wamphamvu
  • Imbirani Yehova Mosangalala
  • Nkhani Yofanana
  • Khalani Maso, Limbani, Khalani Amphamvu
    Imbirani Yehova
  • Dzukani, Chirimikani, Khalani Wamphamvu
    Imbirani Yehova Zitamando
  • “Dikirani”!
    Nsanja ya Olonda—2003
  • Odala Iwo Amene Adikira!
    Nsanja ya Olonda—1997
Onani Zambiri
Imbirani Yehova Mosangalala
sjj nyimbo 126

NYIMBO 126

Khala Maso, Khala Wolimba, Khala Wamphamvu

Losindikizidwa

(1 Akorinto 16:13)

  1. 1. Khala maso, upirire.

    Ukhalebe wamphamvu.

    Ukhale wolimba mtima,

    Udzapambana ndithu.

    Uzimvera mawu a Yesu.

    Ukhalebe ku mbali yake.

    (KOLASI)

    Khala maso, khala wamphamvu.

    Limba mpaka mapeto.

  2. 2. Khala maso, usagone.

    Ukonzeke kumvera,

    Uzimvera malangizo

    Ochokera kwa Yesu.

    Uzimveranso malangizo

    Omwe akulu akupatsa.

    (KOLASI)

    Khala maso, khala wamphamvu.

    Limba mpaka mapeto.

  3. 3. Tikhale ogwirizana

    Poteteza uthenga.

    Ngakhale tizitsutsidwa

    Tizilalikirabe.

    Timutamande mwachimwemwe.

    Tsiku lake layandikira.

    (KOLASI)

    Khala maso, khala wamphamvu.

    Limba mpaka mapeto.

(Onaninso Mat. 24:13; Aheb. 13:​7, 17; 1 Pet. 5:8.)

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena