LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
Baibo ya Cimasulilo ca Dziko Latsopano

Za m’Buku la 1 Atesalonika

1 ATESALONIKA

Za m’Bukuli

  • 1

    • Moni (1)

    • Ayamika Atesalonika cifukwa ca cikhulupililo cao (2-10)

  • 2

    • Utumiki wa Paulo ku Tesalonika (1-12)

    • Atesalonika analandila mau a Mulungu (13-16)

    • Paulo anali kulakalaka kuona Atesalonika (17-20)

  • 3

    • Mwankhawa, Paulo ali ku Atene ndipo ayembekezela lipoti la ku Tesalonika (1-5)

    • Timoteyo abweletsa lipoti lolimbikitsa (6-10)

    • Apemphelela Atesalonika (11-13)

  • 4

    • Awacenjeza kuti azipewa ciwelewele (1-8)

    • Mupitilize kukondana kwambili (9-12)

      • “Musamalowelele nkhani za ena” (11)

    • Amene anafa mwa Khristu adzakhala oyambilila kuuka (13-18)

  • 5

    • Kubwela kwa tsiku la Yehova (1-5)

      • “Bata ndi mtendele!” (3)

    • Khalani maso ndipo khalani oganiza bwino (6-11)

    • Kuwalimbikitsa (12-24)

    • Moni womaliza (25-28)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2026)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani