LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w15 4/15 masa. 1-2
  • Zamkati

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zamkati
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • Tumitu
  • YOPHUNZILA
  • NKHANI ZOPHUNZILA
  • NKHANI ZINA M’MAGAZINI INO
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
w15 4/15 masa. 1-2

Zamkati

April 15, 2015

© 2015 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

YOPHUNZILA

JUNE 1-7, 2015

Akulu, Kodi Mumakonda Kuphunzitsa Ena?

TSAMBA 3 • NYIMBO: 123, 121

JUNE 8-14, 2015

Mmene Akulu Angathandizile Ena Kukhala Oyenelela Maudindo

TSAMBA 9 • NYIMBO: 45, 70

JUNE 15-21, 2015

Kodi Muli pa Ubwenzi Wolimba ndi Yehova?

TSAMBA 19 • NYIMBO: 91, 11

JUNE 22-28, 2015

Muzikhulupilila Yehova Nthawi Zonse

TSAMBA 24 • NYIMBO: 106, 49

NKHANI ZOPHUNZILA

▪ Akulu, Kodi Mumakonda Kuphunzitsa Ena?

▪ Mmene Akulu Angathandizile Ena Kukhala Oyenelela Maudindo

N’cifukwa ciani akulu afunika kuphunzitsa ena mumpingo? Nanga ndi zinthu ziti zimene akulu ayenela kucita kuti akwanitse kuphunzitsa ena? Kodi akulu ndiponso abale ena amene amaphunzitsidwa ndi akulu angaphunzile ciani kwa Samueli, Eliya, ndi Elisa? Nkhani ziŵilizi zikuyankha mafunso amenewa.

▪ Kodi Muli pa Ubwenzi Wolimba ndi Yehova?

▪ Muzikhulupilila Yehova Nthawi Zonse

Kukhala pa ubwenzi wabwino ndi Yehova kudzatithandiza kupilila mayeselo. Nkhani ziŵilizi zifotokoza mmene kukambilana ndi Yehova ndiponso kumudalila nthawi zonse kumalimbitsila ubwenzi wathu ndi iye.

NKHANI ZINA M’MAGAZINI INO

14 Madalitso “m’Nthawi Yabwino ndi m’Nthawi Yovuta”

29 Cifukwa Cake Kucotsa Munthu Mumpingo Ndi Makonzedwe Acikondi

32 Kodi Mtengo Ukadulidwa Ungaphukenso?

PACIKUTO: Mkulu akuphunzitsa mtumiki wothandiza kucita ulaliki wapoyela wa m’mizinda ikuluikulu m’mbali mwa mseu wochedwa Haiphong Road, mumzinda wa Kowloon

HONG KONG

KULI ANTHU

7,234,800

OFALITSA

5,747

MAPHUNZILO A BAIBULO

6,382
Cithunzi papeji 2
ZOPOSA 180,000

Mashelufu a mawilo, matebulo, ndi zinthu zina zoikapo mabuku zinagulidwa kudzela mu ofesi ya nthambi ya ku Hong Kong ndi kutumizidwa padziko lonse

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani