LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • w15 6/15 masa. 1-2
  • Zamkati

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Zamkati
  • Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
  • Tumitu
  • YOPHUNZILA
  • NKHANI ZOPHUNZILA
  • NKHANI ZINA M’MAGAZINI INO
Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2015
w15 6/15 masa. 1-2

Zamkati

June 15, 2015

© 2015 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania

YOPHUNZILA

JULY 27, 2015–AUGUST 2, 2015

Kristu Ndiye Mphamvu ya Mulungu

TSAMBA 3 • NYIMBO: 14, 109

AUGUST 3-9, 2015

Anali Kukonda Anthu

TSAMBA 8 • NYIMBO: 84, 99

AUGUST 10-16, 2015

Tingathe Kupewa Ciwelewele

TSAMBA 13 • NYIMBO: 83, 57

AUGUST 17-23, 2015

Muzicita Zinthu Mogwilizana ndi Pemphelo Lacitsanzo—Mbali 1

TSAMBA 20 • NYIMBO: 138 Inu Ndinu Yehova (nyimbo yatsopano), 89

AUGUST 24-30, 2015

Muzicita Zinthu Mogwilizana ndi Pemphelo Lacitsanzo—Mbali 2

TSAMBA 25 • NYIMBO: 22, 68

NKHANI ZOPHUNZILA

▪ Kristu Ndiye Mphamvu ya Mulungu

▪ Anali Kukonda Anthu

Nkhanizi zikufotokoza zozizwitsa za Yesu. Zikutiphunzitsa kukhala oolowa manja ndi kukhala ndi mtima wofuna kuthandiza ena, ndiponso zikufotokoza mbali zocititsa cidwi za umunthu wake. Zikutionetsanso kuti posacedwapa tidzaona zozizwitsa zambili zikucitika padziko lonse.

▪ Tingathe Kupewa Ciwelewele

Popeza tikukhala m’dziko limene limalimbikitsa ciwelewele, zingakhale zovuta kupewa mkhalidwe woipa umenewu. Nkhaniyi itionetsa mmene ubwenzi wathu ndi Yehova, malangizo a m’Baibulo, ndi thandizo la Akristu anzathu zingatithandizile kupewa zilakolako zoipa. Ndiponso itithandiza kutsatila mfundo zapamwamba za Yehova.

▪ Muzicita Zinthu Mogwilizana ndi Pemphelo Lacitsanzo—Mbali 1

▪ Muzicita Zinthu Mogwilizana ndi Pemphelo Lacitsanzo—Mbali 2

Akristu sabweleza pemphelo lacitsanzo la Yesu, koma mapempho a m’pempheloli ali ndi tanthauzo kwa ife. Nkhani ziŵilizi zitithandiza kuona mmene tingacitile zinthu mogwilizana ndi mapempho amenewo.

NKHANI ZINA M’MAGAZINI INO

18 “Ngati Kingsley Wakwanitsa Inenso Ndingakwanitse”

30 “Mukufunika Kupilila”

32 Kodi Mukukumbukila?

PACIKUTO: Mboni za Yehova zimagwilitsila nchito maboti kuti zikalalikile anthu amene amakhala ku zilumba za Bocas del Toro ndi Archipelago kumpoto cakumadzulo kwa dziko la Panama. Zimalalikilanso m’cinenelo ca Cingabere

KU PANAMA

KULI ANTHU

3,931,000

OFALITSA

16,217

APAINIYA

2,534

M’mipingo 309 ya ku Panama, muli apainiya apadela oposa 180. Ofalitsa pafupifupi 1,100 amatumikila m’mipingo 35 ndi m’tumagulu 15 ndipo amagwilitsila nchito cinenelo ca Cingabere. Kulinso ofalitsa pafupifupi 600 amene amatumikila m’mipingo 16 komanso tumagulu 6 ndipo amagwilitsila nchito cinenelo Camanja ca ku Panama

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani