LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 4/13 tsa. 3
  • Ndandanda ya Mlungu wa April 22

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa April 22
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Tumitu
  • MLUNGU WA APRIL 22
Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
km 4/13 tsa. 3

Ndandanda ya Mlungu wa April 22

MLUNGU WA APRIL 22

Nyimbo 85 ndi Pemphelo

□ Phunzilo la Baibo la Mpingo:

bt mutu 22 ndime 1 mpaka 6 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibo: Luka 18-21 (Mph. 10)

Na. 1: Luka 18:18-34 (Mph. 4 kapena zocepelapo)

Na. 2: Kodi Zidzathekadi Kuti Anthu a Mitundu Yonse Adzagwilizane Monga Abale ndi Alongo?—rs tsa. 238 ndime 1-tsa. 239 ndime 1 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Kufatsa N’kutani, N’cifukwa Ciani Khalidwe Limeneli Lili Lofunika Ndipo Tingatani Kuti Tikhale Nalo?—Zef. 2:2, 3 (Mph. 5)

□ Msonkhano wa Nchito:

Nyimbo 120

Mph. 10: “Zimene Mungacite kuti Lipoti Likhale Lolondola.” Nkhani yokambidwa ndi mkulu yocokela m’buku la Gulu, patsamba 85 ndime 1 mpaka 87 ndime 1. Mukambe nkhaniyi malinga ndi zosoŵa za mpingo, ndipo unikani kufunika kopeleka lipoti lolondola. Yamikilani abale kaamba ka khama lao muulaliki.

Mph. 20: Gwilitsilani Nchito Baibo Mwaluso Muulaliki. Nkhani yokambilana yocokela mu Nsanja ya Olonda ya February 15, 2010, masamba 13 ndi 14 ndime 14 mpaka 17. Pokambilana ndime 15, mukhale ndi citsanzo coonetsa wofalitsa akugwilitsila nchito Baibo mwaluso muulaliki.

Nyimbo 121 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani